1
Ezekieli 13:3
Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
CCL
Ambuye Yehova akuti, ‘Tsoka kwa aneneri opusa amene amangonenera zopeka ngakhale kuti sanaone kanthu konse!’
Compare
Explore Ezekieli 13:3
2
Ezekieli 13:6
Masomphenya awo ndi achabe ndipo kuwombeza kwawo ndi kwabodza. Iwo amati, ‘Yehova akutero,’ pomwe Yehova sanawatume. Komabe iwo amayembekezera kuti zimene ayankhulazo zichitikadi.
Explore Ezekieli 13:6