1
Matayo 26:41
Nyanja
NTNYBL2025
Chezelani ni kupembhela kuti msadalowa mu mayeselo. Mtima ufuna kuchita yayo yafunika, nambho thupi lilibe mbhavu.”
Linganisha
Chunguza Matayo 26:41
2
Matayo 26:38
Kumeneko wadaakambila, “Nili ni chisoni chachikulu mumtima mwanga icho chikhoza kunipha. Khalani pano ni muchezele pamojhi ni ine.”
Chunguza Matayo 26:38
3
Matayo 26:39
Wadapita pachogolo pang'ono, wadagwa panjhi chifufumimba ni kupembhela, “Atate wanga, ngati ikhozeka, nichocheleni chikho ichi cha mavuto! Chipano osati ngati umo nifunila ine, nambho ngati umo mufunila imwe.”
Chunguza Matayo 26:39
4
Matayo 26:28
uwu nde mwazi wanga uwo uchimikiza chipangano, umwazika ndande ya ambili dala machimo yao yalekeleledwe.
Chunguza Matayo 26:28
5
Matayo 26:26
Yapo amadya Yesu wadatenga bumunda, wadayamika, wadaubandhula, ni kwapacha oyaluzidwa wake nikukamba, “Tengani mudye, ili nithupi langa.”
Chunguza Matayo 26:26
6
Matayo 26:27
Ndiipo wadatenga chikho, wadayamika Mnungu, ni kwaapacha oyaluzidwa wake niwakamba, “Mwaonjhe mchimwele chikho ichi
Chunguza Matayo 26:27
7
Matayo 26:40
Ndiipo wadabwela kwa oyaluzidwa wake ni kwaapheza agona, wadamkambila Petulo, “Ikhala bwanji simdakhoze kuchezelela ni ine ata kwa saa imojhipe?
Chunguza Matayo 26:40
8
Matayo 26:29
Nikukambilani, sinimwanjho divai iyi mbaka siku ilo sinimwe divai yachipano ni anyiimwe mu Ufumu wa Atate wanga.”
Chunguza Matayo 26:29
9
Matayo 26:75
Ndiipo Petulo wadakumbukila mau yajha wadakamba Yesu, “Tambala wakali osalile, siunikane katatu.” Wadapita kubwalo, wadalila kwa kubuula.
Chunguza Matayo 26:75
10
Matayo 26:46
Imani tijhipita. Yujha waning'anamuka watokujha.”
Chunguza Matayo 26:46
11
Matayo 26:52
Ndiipo Yesu wadamkambila, “Bwezela upanga wako mmalo mwake, pakuti waliyonjhe wakupha kwa upanga, siwaphedwe kwa upanga.
Chunguza Matayo 26:52
Nyumbani
Biblia
Mipango
Video