1
ZEKARIYA 7:9
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
Watero Yehova wa makamu, kuti, Weruzani chiweruzo choona, nimuchitire yense mnzake chifundo ndi ukoma mtima
Linganisha
Chunguza ZEKARIYA 7:9
2
ZEKARIYA 7:10
musazunza mkazi wamasiye, kapena ana amasiye, mlendo kapena waumphawi; ndipo nnena mmodzi wa inu alingirire m'mtima mwake kumchitira choipa munthu mnzake.
Chunguza ZEKARIYA 7:10
Nyumbani
Biblia
Mipango
Video