1
ZEKARIYA 6:12
Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014
BLPB2014
nunene naye, kuti, Atero Yehova wa makamu, ndi kuti, Taonani, munthu dzina lake ndilo Mphukira, ndipo adzaphuka m'malo mwake, nadzamanga Kachisi wa Yehova
Linganisha
Chunguza ZEKARIYA 6:12
2
ZEKARIYA 6:13
inde adzamanga Kachisi wa Yehova; nadzasenza ulemererowo, nadzakhala ndi kulamulira pa mpando wachifumu wake; nadzakhala wansembe pampando wachifumu wake; ndi uphungu wa mtendere udzakhala pakati pa iwo awiri.
Chunguza ZEKARIYA 6:13
Nyumbani
Biblia
Mipango
Video