1
Mt. 3:8
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
BLY-DC
Chitanitu ntchito zosonyeza kuti mwatembenukadi mtima.
مقایسه
Mt. 3:8 را جستجو کنید
2
Mt. 3:17
Tsono kuthamboko kudamveka mau akuti, “Uyu ndiye Mwana wanga wapamtima. Ndimakondwera naye kwambiri.”
Mt. 3:17 را جستجو کنید
3
Mt. 3:16
Yesu atangobatizidwa, adatuluka m'madzimo. Pomwepo kuthambo kudatsekuka, ndipo adaona Mzimu wa Mulungu akutsika ngati nkhunda nkutera pa Iye.
Mt. 3:16 را جستجو کنید
4
Mt. 3:11
“Ine ndimakubatizani ndi madzi, kusonyeza kuti mwatembenuka mtima. Koma amene akubwera pambuyo panga ndi wamphamvu kuposa ine. Ameneyo ine ndine wosayenera ngakhale kunyamula nsapato zake. Iyeyo adzakubatizani mwa Mzimu Woyera ndiponso m'moto.
Mt. 3:11 را جستجو کنید
5
Mt. 3:10
Pali pano nkhwangwa ili kale patsinde pa mitengo. Choncho mtengo uliwonse wosabala zipatso zabwino, adzaudula nkuuponya pa moto.
Mt. 3:10 را جستجو کنید
6
Mt. 3:3
Paja Yesaya ankanena za iyeyu pamene adaati, “Liwu la munthu wofuula m'chipululu: akunena kuti, ‘Konzani mseu wodzadzeramo Ambuye, ongolani njira zoti adzapitemo.’ ”
Mt. 3:3 را جستجو کنید