1
Lk. 2:11
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
BLY-DC
Usiku womwe uno m'mudzi wa Davide wakubadwirani Mpulumutsi, amene ndi Khristu Ambuye.
مقایسه
Lk. 2:11 را جستجو کنید
2
Lk. 2:10
Koma mngeloyo adaŵauza kuti, “Musaope, ndadzakuuzani uthenga wabwino, umene udzakondweretsa anthu onse kwambiri.
Lk. 2:10 را جستجو کنید
3
Lk. 2:14
“Ulemerero kwa Mulungu Kumwambamwamba, ndipo pansi pano mtendere pakati pa anthu amene Iye amakondwera nawo.”
Lk. 2:14 را جستجو کنید
4
Lk. 2:52
Ndipo Yesu analikunka nakula m'nzeru ndi mu msinkhu, ndipo Mulungu ndi anthu omwe ankakondwera naye kwambiri.
Lk. 2:52 را جستجو کنید
5
Lk. 2:12
Chitsimikizo chake ndi ichi: mukapeza mwana wakhanda, wokutidwa ndi nsalu, atagona m'chodyera cha zoŵeta.”
Lk. 2:12 را جستجو کنید
6
Lk. 2:8-9
Ku dera lomwelo kunali abusa amene ankalonda zoŵeta zao ku dambo usiku. Mwadzidzidzi mngelo wa Ambuye adadzaimirira pakati pao, ndipo ulemerero wa Ambuye udaŵala ponse pozungulira, mwakuti abusawo adaachita mantha kwambiri.
Lk. 2:8-9 را جستجو کنید