1
Lk. 12:40
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
BLY-DC
Choncho inunso khalani okonzeka, pakuti Mwana wa Munthu adzabwera pa nthaŵi imene simukuyembekeza.”
مقایسه
Lk. 12:40 را جستجو کنید
2
Lk. 12:31
Koma inu, yambani mwafunafuna ufumu wa Mulungu, ndipo zina zonsezi adzakupatsaninso.”
Lk. 12:31 را جستجو کنید
3
Lk. 12:15
Atatero adauza anthu aja kuti, “Chenjerani, ndipo mupewe khumbo lililonse lofuna zambiri. Pajatu ngakhale munthu akhale ndi chuma chochuluka chotani, chumacho sichingatchinjirize moyo wake.”
Lk. 12:15 را جستجو کنید
4
Lk. 12:34
Pajatu kumene kuli chuma chako, mtima wakonso kokhala nkomweko.”
Lk. 12:34 را جستجو کنید
5
Lk. 12:25
Ndani mwa inu ndi maganizo ankhaŵa angathe kuwonjezera ngakhale tsiku limodzi pa moyo wake?
Lk. 12:25 را جستجو کنید
6
Lk. 12:22
Yesu adauza ophunzira ake kuti, “Nchifukwa chake ndikukuuzani kuti musamadera nkhaŵa moyo wanu, kuti mudzadyanji, kapena thupi lanu, kuti mudzavalanji.
Lk. 12:22 را جستجو کنید
7
Lk. 12:7
Ndipo tsitsi lomwe la kumutu kwanu adaliŵerenga lonse. Choncho musati muziwopa ai. Ndinu a mtengo woposa atimba ambiri.”
Lk. 12:7 را جستجو کنید
8
Lk. 12:32
“Inu nkhosa zanga, ngakhale muli oŵerengeka, musaope, pakuti kudakomera Atate anu kuti akupatseni Ufumu wake.
Lk. 12:32 را جستجو کنید
9
Lk. 12:24
Onani makwangwala. Safesa, sakolola, alibe nyumba yosungiramo zinthu, kapena nkhokwe, komabe Mulungu amaŵadyetsa. Inu mumazipambana mbalamezo kutali.
Lk. 12:24 را جستجو کنید
10
Lk. 12:29
Nchifukwa chake musamadera nkhaŵa ndi kufunafuna zoti mudye, kapena zoti mumwe.
Lk. 12:29 را جستجو کنید
11
Lk. 12:28
Tsono ngati Mulungu amaveka motere udzu wakuthengo, umene ungokhalapo lero lokha, maŵa lino nkuponyedwa pa moto, nanji inuyo, angapande kukuvekani, inu a chikhulupiriro chochepanu?
Lk. 12:28 را جستجو کنید
12
Lk. 12:2
Kanthu kalikonse kovundikirika kadzaululuka, ndipo kalikonse kobisika kadzadziŵika.
Lk. 12:2 را جستجو کنید