1
Lk. 10:19
Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa
BLY-DC
Ndakupatsanitu mphamvu kuti muziponda njoka ndi zinkhanira, ndi kumagonjetsa mphamvu zonse za mdani uja. Palibe kanthu kamene kangakupwetekeni.
مقایسه
Lk. 10:19 را جستجو کنید
2
Lk. 10:41-42
Ambuye adati, “Iwe Marita iwe, ukutekeseka nkuvutika ndi zinthu zambiri, koma chofunika nchimodzi chokha. Maria ndiye wasankhula chinthu chopambana, ndipo chimenechi palibe wina angamlande ai.”
Lk. 10:41-42 را جستجو کنید
3
Lk. 10:27
Iye adayankha kuti, “Uzikonda Chauta, Mulungu wako, ndi mtima wako wonse, ndi moyo wako wonse, ndi mphamvu zako zonse, ndi nzeru zako zonse, ndiponso mnzako monga momwe umadzikondera iwe wemwe.”
Lk. 10:27 را جستجو کنید
4
Lk. 10:2
Adaŵauza kuti, “Dzinthu ndzambiri, koma antchito ngochepa. Nchifukwa chake pemphani Mwini dzinthu kuti atume antchito kukatuta dzinthudzo.
Lk. 10:2 را جستجو کنید
5
Lk. 10:36-37
Tsono Yesu adafunsa katswiri wa Malamulo uja kuti, “Inu pamenepa mukuganiza bwanji? Mwa anthu atatuŵa, ndani adakhala ngati mnzake wa munthu uja achifwamba adaamugwirayu?” Iye adati, “Amene adamchitira chifundo uja.” Apo Yesu adamuuza kuti, “Pitani tsono, nanunso muzikachita chimodzimodzi.”
Lk. 10:36-37 را جستجو کنید
6
Lk. 10:3
Pitani tsono. Ndikukutumani ngati anaankhosa pakati pa mimbulu.
Lk. 10:3 را جستجو کنید