1
LUKA 2:11
Buku Lopatulika
BLP-2018
pakuti wakubadwirani inu lero, m'mzinda wa Davide, Mpulumutsi, amene ali Khristu Ambuye.
مقایسه
LUKA 2:11 را جستجو کنید
2
LUKA 2:10
Ndipo mngelo anati kwa iwo, Musaope; pakuti onani, ndikuuzani inu uthenga wabwino wa chikondwero chachikulu, chimene chidzakhala kwa anthu onse
LUKA 2:10 را جستجو کنید
3
LUKA 2:14
Ulemerero ukhale kwa Mulungu Kumwambamwamba, ndi mtendere pansi pano mwa anthu amene akondwera nao.
LUKA 2:14 را جستجو کنید
4
LUKA 2:52
Ndipo Yesu anakulabe m'nzeru ndi mumsinkhu, ndi m'chisomo cha pa Mulungu ndi cha pa anthu.
LUKA 2:52 را جستجو کنید
5
LUKA 2:12
Ndipo ichi ndi chizindikiro kwa inu: Mudzapeza mwana wakhanda wokuta ndi nsalu atagona modyera.
LUKA 2:12 را جستجو کنید
6
LUKA 2:8-9
Ndipo panali abusa m'dziko lomwelo, okhala kubusa ndi kuyang'anira zoweta zao usiku. Ndipo mngelo wa Ambuye anaimirira pa awo, ndi kuwala kwa Ambuye kunawaunikira kozungulira: ndipo anaopa ndi mantha aakulu.
LUKA 2:8-9 را جستجو کنید