لوگو یوورژن
كتاب‌ مقدسبرنامه‌های مطالعهویدیوها
دانلود برنامه
انتخاب زبان
ایکن جستجو

آیات محبوب کتاب مقدس از YOHANE 2

1

YOHANE 2:11

Buku Lopatulika

BLP-2018

Chiyambi ichi cha zizindikiro zake Yesu anachita mu Kana wa mu Galileya naonetsera ulemerero wake; ndipo ophunzira ake anakhulupirira Iye.

مقایسه

YOHANE 2:11 را جستجو کنید

2

YOHANE 2:4

Buku Lopatulika

BLP-2018

Yesu nanena naye, Mkazi, ndili ndi chiyani ndi inu? Nthawi yanga siinafike.

مقایسه

YOHANE 2:4 را جستجو کنید

3

YOHANE 2:7-8

Buku Lopatulika

BLP-2018

Yesu ananena nao, Dzazani mitsukoyo ndi madzi. Naidzaza, ndendende. Ndipo ananena nao, Tungani tsopano, mupite nao kwa mkulu wa phwando. Ndipo anapita nao.

مقایسه

YOHANE 2:7-8 را جستجو کنید

4

YOHANE 2:19

Buku Lopatulika

BLP-2018

Yesu anayankha nati kwa iwo, Pasulani Kachisi uyu, ndipo masiku atatu ndidzamuutsa.

مقایسه

YOHANE 2:19 را جستجو کنید

5

YOHANE 2:15-16

Buku Lopatulika

BLP-2018

Ndipo pamene adapanga mkwapulo wazingwe, anatulutsa onse mu Kachisimo, ndi nkhosa ndi ng'ombe; nakhuthula ndalama za osinthanawo, nagubuduza magome; nati kwa iwo akugulitsa nkhunda, Chotsani izi muno; musamayesa nyumba ya Atate wanga nyumba ya malonda.

مقایسه

YOHANE 2:15-16 را جستجو کنید

برنامه های خواندنی رایگان و عبادات مربوط به YOHANE 2

باب‌ قبلی
باب بعدی
یوورژن

به چالش کشیدن و تشویق هر روزه شما برای ایجاد رابطه صمیمی تر با خدا .

خدمت

دربارهٔ

مشاغل

داوطلب شوید.

بلاگ

مطبوعات

لینک‌های مفید

پشتیبانی

اهدای کمک مالی

ترجمه‌های کتاب‌مقدس

کتاب‌ مقدس صوتی

ترجمه‌های موجود کتاب‌مقس

آیۀ روز


یک خدمت دیجیتالی از

لایف‌چرچ
English (US)

©2025 لایف چرچ / یوورژن

قوانین حفظ حریم شخصیشرايط
برنامه افشای آسیب پذیری
فیس‌بوکتویتراینستاگرامبرنامه یوتیوببرنامه پین ترست

خانه

كتاب‌ مقدس

برنامه‌های مطالعه

ویدیوها