YouVersion Logo
Search Icon

Mk. 16:17-18

Mk. 16:17-18 BLY-DC

Okhulupirira azidzachita zozizwitsa izi: azidzatulutsa mizimu yoipa potchula dzina langa, azidzalankhula zilankhulo zachilendo, ndipo akagwira njoka kapena kumwa chakumwa chotha kuŵapha, sadzapwetekedwa. Akasanjika manja pa anthu odwala, anthuwo azidzachira.”

Free Reading Plans and Devotionals related to Mk. 16:17-18