Mt. 15:25-27
Mt. 15:25-27 BLY-DC
Mai uja adadzamgwadira nati, “Ambuye, ndithu thandizeni.” Yesu adamuuza kuti, “Sibwino kutenga chakudya cha ana nkuponyera agalu.” Maiyo adati, “Nzoonadi, Ambuye, koma suja ngakhale agalu omwe amadyako nyenyeswa zimene zimagwa pansi kuchokera pa tebulo la mbuye ao?”





