YouVersion Logo
Search Icon

Mt. 15:18-19

Mt. 15:18-19 BLY-DC

Koma zotuluka m'kamwa mwa munthu zimachokera mu mtima, ndipo zimenezi ndizo zimamuipitsa. Chifukwa m'kati mwa mitima ya anthu ndiye mumatuluka maganizo oipa, za kuphana, za chigololo, za chiwerewere, za kuba, maumboni onama, ndiponso zachipongwe.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mt. 15:18-19