YouVersion Logo
Search Icon

Mal. 2:15

Mal. 2:15 BLY-DC

Kodi suja Mulungu adakulenga, iwe ndi mkazi wako, kukhala mmodzi, thupi ndi mzimu womwe? Nanga pakutero Mulunguyo ankafuna chiyani? Ankafunatu ana ompembedza Iye. Motero samala moyo wako ndipo khala wokhulupirika kwa mkazi wako woyamba.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mal. 2:15