YouVersion Logo
Search Icon

Lk. 3:8

Lk. 3:8 BLY-DC

Chitanitu ntchito zosonyeza kuti mwatembenukadi mtima. Ndipo m'mitima mwanu musayambe zomanena kuti, ‘Atate athu ndi Abrahamu.’ Ndithu ndikunenetsa kuti Mulungu angathe kusandutsa ngakhale miyala ili apayi kuti ikhale ana a Abrahamu.

Free Reading Plans and Devotionals related to Lk. 3:8