YouVersion Logo
Search Icon

AROMA 12:2

AROMA 12:2 BLPB2014

Ndipo musafanizidwe ndi makhalidwe a pansi pano: koma mukhale osandulika, mwa kukonzanso kwa mtima wanu, kuti mukazindikire chimene chili chifuno cha Mulungu, chabwino, ndi chokondweretsa, ndi changwiro.

Free Reading Plans and Devotionals related to AROMA 12:2