YouVersion Logo
Search Icon

MARKO 4:26-27

MARKO 4:26-27 BLPB2014

Ndipo ananena, Ufumu wa Mulungu uli wotero, monga ngati munthu akataya mbeu panthaka; nakagona ndi kuuka, usiku ndi usana, ndipo mbeu zikamera, ndi kukula, iye sadziwa umo zichitira.