YouVersion Logo
Search Icon

MATEYU 9:37-38

MATEYU 9:37-38 BLPB2014

Pomwepo ananena kwa ophunzira ake, Zotuta zichulukadi koma antchito ali owerengeka. Chifukwa chake pempherani Mwini zotuta kuti akokose antchito kukututa kwake.