YouVersion Logo
Search Icon

MATEYU 4:1-2

MATEYU 4:1-2 BLPB2014

Pamenepo Yesu anatengedwa ndi Mzimu kunka kuchipululu kukayesedwa ndi mdierekezi. Ndipo pamene Iye analibe kudya masiku makumi anai usana ndi usiku, pambuyo pake anamva njala.

Free Reading Plans and Devotionals related to MATEYU 4:1-2