YouVersion Logo
Search Icon

HOSEYA 9:7

HOSEYA 9:7 BLPB2014

Masiku a kulanga afika, masiku a kubwezera afika; Israele adzadziwa; mneneri ali wopusa, munthu wamzimu ali wamisala, chifukwa cha kuchuluka mphulupulu yako, ndi popeza udani ndi waukulu.

Related Videos

Free Reading Plans and Devotionals related to HOSEYA 9:7