YouVersion Logo
Search Icon

EKSODO 31:17

EKSODO 31:17 BLPB2014

ndicho chizindikiro chosatha pakati pa Ine ndi ana a Israele; pakuti Yehova analenga zam'mwamba ndi dziko lapansi masiku asanu ndi limodzi, napumula tsiku lachisanu ndi chiwiri, naonanso mphamvu.

Free Reading Plans and Devotionals related to EKSODO 31:17