YouVersion Logo
Search Icon

EKSODO 31:13

EKSODO 31:13 BLPB2014

Koma iwe, lankhula ndi ana a Israele, ndi kuti, Muzisunga masabata anga ndithu; pakuti ndiwo chizindikiro pakati pa Ine ndi inu mwa mibadwo yanu; kuti mudziwe kuti Ine ndine Yehova wakukupatulani.

Free Reading Plans and Devotionals related to EKSODO 31:13