YouVersion Logo
Search Icon

2 MAFUMU 6:15

2 MAFUMU 6:15 BLPB2014

Ndipo atalawirira mamawa mnyamata wa munthu wa Mulungu, natuluka, taonani, khamu la nkhondo linazinga mudzi ndi akavalo ndi magaleta. Ndi mnyamata wake ananena naye, Kalanga ine, mbuye wanga! Tichitenji?

Free Reading Plans and Devotionals related to 2 MAFUMU 6:15