YouVersion Logo
Search Icon

2 AKORINTO 6:16

2 AKORINTO 6:16 BLPB2014

Ndipo chiphatikizo chake nchanji ndi Kachisi wa Mulungu ndi wa mafano? Pakuti ife ndife Kachisi wa Mulungu wamoyo; monga Mulungu anati, Ndidzakhalitsa mwa iwo, ndipo ndidzayendayenda mwa iwo; ndipo ndidzakhala Mulungu wao, ndi iwo adzakhala anthu anga.

Free Reading Plans and Devotionals related to 2 AKORINTO 6:16