YouVersion Logo
Search Icon

1 PETRO 3:3-4

1 PETRO 3:3-4 BLPB2014

Amene kukometsera kwanu kusakhale kwa kunja, kuluka tsitsi ndi kuvala za golide, kapena kuvala chovala; koma kukhale munthu wobisika wamtima, m'chovala chosaola cha mzimu wofatsa ndi wachete, ndiwo wa mtengo wake wapatali pamaso pa Mulungu.

Free Reading Plans and Devotionals related to 1 PETRO 3:3-4