YouVersion Logo
Search Icon

1 AKORINTO 6:19-20

1 AKORINTO 6:19-20 BLPB2014

Kapena simudziwa kuti thupi lanu lili Kachisi wa Mzimu Woyera, amene ali mwa inu, amene muli naye kwa Mulungu? Ndipo simukhala a inu nokha. Pakuti munagulidwa ndi mtengo wake wapatali; chifukwa chake lemekezani Mulungu m'thupi lanu.

Free Reading Plans and Devotionals related to 1 AKORINTO 6:19-20