YouVersion Logo
Search Icon

Miyambo 23:5

Miyambo 23:5 CCL

Ukangoti wachipeza chumacho uwona posachedwa kuti palibepo. Chumacho chimachita ngati chamera mapiko mwadzidzidzi ndi kuwuluka kunka kumwamba ngati chiwombankhanga.

Free Reading Plans and Devotionals related to Miyambo 23:5