YouVersion Logo
Search Icon

Afilipi 3:10-11

Afilipi 3:10-11 CCL

Ine ndikufuna kudziwa Khristu, ndithu, kudziwa mphamvu zake za kuuka kwa akufa. Ndikufuna kuyanjana naye mʼmasautso ake, kufanana naye pa imfa yake kuti nanenso ndidzaukitsidwe kwa akufa.

Free Reading Plans and Devotionals related to Afilipi 3:10-11