YouVersion Logo
Search Icon

Numeri 22:32

Numeri 22:32 CCL

Mngelo wa Yehova anamufunsa kuti, “Chifukwa chiyani wamenya bulu wako katatu? Taona, Ine ndabwera kudzakutsutsa chifukwa ulendo wakowu ndi woyipa pamaso panga.

Video for Numeri 22:32

Free Reading Plans and Devotionals related to Numeri 22:32