YouVersion Logo
Search Icon

Marko 4:26-27

Marko 4:26-27 CCL

Iye anatinso, “Umu ndi mmene ulili ufumu wa Mulungu. Munthu amafesa mbewu mʼnthaka. Usiku ndi usana, kaya agona kapena adzuka, mbewu imamera ndi kukula, ngakhale sadziwa mmene zimachitikira.

Free Reading Plans and Devotionals related to Marko 4:26-27