YouVersion Logo
Search Icon

Mika 2:12

Mika 2:12 CCL

“Inu banja la Yakobo, ndidzakusonkhanitsani nonse; ndidzawasonkhanitsa pamodzi otsala a ku Israeli. Ndidzawabweretsa pamodzi ngati nkhosa mʼkhola, ngati ziweto pa msipu wake; malowo adzadzaza ndi chinamtindi cha anthu.

Related Videos

Free Reading Plans and Devotionals related to Mika 2:12