YouVersion Logo
Search Icon

Luka 5:5-6

Luka 5:5-6 CCL

Simoni anayankha kuti, “Ambuye, tagwira ntchito molimbika usiku wonse, koma sitinagwire kanthu. Koma pakuti mwatero, ndiponya makhoka.” Atachita izi, anagwira nsomba zambiri kotero kuti makhoka awo anayamba kungʼambika.

Free Reading Plans and Devotionals related to Luka 5:5-6