YouVersion Logo
Search Icon

Levitiko 26:5

Levitiko 26:5 CCL

Mudzakhala mukupuntha tirigu mpaka nthawi yothyola mphesa, ndipo mudzakhala mukuthyola mphesa mpaka nthawi yodzala. Mudzadya chakudya chanu mpaka kukhuta ndipo mudzakhala mʼdziko lanu mwamtendere.

Free Reading Plans and Devotionals related to Levitiko 26:5