YouVersion Logo
Search Icon

Yeremiya 24:7

Yeremiya 24:7 CCL

Ndidzawapatsa mtima woti andidziwe kuti ndine Yehova. Adzakhala anthu anga ndipo Ine ndidzakhala Mulungu wawo, chifukwa adzabwerera kwa Ine ndi mtima wawo wonse.

Video for Yeremiya 24:7