YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 9:3

Yesaya 9:3 CCL

Inu mwauchulukitsa mtundu wanu ndipo mwawonjezera chimwemwe chawo. Iwo akukondwa pamaso panu, ngati mmene anthu amakondwera nthawi yokolola, ngatinso mmene anthu amakondwera pamene akugawana zolanda ku nkhondo.

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 9:3