YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 38:1

Yesaya 38:1 CCL

Nthawi imeneyo Mfumu Hezekiya anadwala ndipo anali pafupi kufa. Mneneri Yesaya mwana wa Amozi anapita kukamuona ndipo anati “Yehova akuti: Konza bwino nyumba yako, pakuti ukufa; suchira.”

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 38:1