Yesaya 35:3-4
Yesaya 35:3-4 CCL
Limbitsani manja ofowoka, limbitsani mawondo agwedegwede; nenani kwa a mitima yamantha kuti; “Limbani mtima, musachite mantha; Mulungu wanu akubwera, akubwera kudzalipsira; ndi kudzabwezera chilango adani anu; akubwera kudzakupulumutsani.”





