YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 31:2

Yesaya 31:2 CCL

Komatu Yehovayo ndi wanzeru ndipo angathe kuwononga, ndipo sasintha chimene wanena. Adzalimbana ndi anthu ochita zoyipa, komanso ndi amene amathandiza anthu ochita zoyipa.

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 31:2