YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 30:15

Yesaya 30:15 CCL

Zimene Ambuye Yehova, Woyerayo wa Israeli ananena ndi izi: “Ngati mubwerera ndi kupuma mudzapulumuka, ngati mukhala chete ndi kukhulupirira mudzakhala amphamvu, koma inu munakana zimenezi.

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 30:15