YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 30:1

Yesaya 30:1 CCL

Yehova akuti, “Tsoka kwa ana ondipandukira amene amachita zowakomera iwo okha osati Ine, nachita mgwirizano wawowawo koma osati motsogozedwa ndi Ine. Choncho amanka nachimwirachimwira.

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 30:1