YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 29:16

Yesaya 29:16 CCL

Inu mumazondotsa zinthu ngati kuti dothi lasanduka wowumba mbiya. Kodi chinthu chopangidwa chingawuze wochipanga kuti “Sunandipange ndi iwe?” Kapena mʼphika kunena kwa amene anawuwumba kuti, “Iwe sudziwa chilichonse?”

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 29:16