YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 14:13

Yesaya 14:13 CCL

Mu mtima mwako unkanena kuti, “Ndidzakwera mpaka kumwamba; ndidzakhazika mpando wanga waufumu pamwamba pa nyenyezi za Mulungu; ndidzakhala pa mpando waufumu pa phiri losonkhanirako, pamwamba penipeni pa phiri la kumpoto.

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 14:13