YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 12:4

Yesaya 12:4 CCL

Tsiku limenelo mudzati: “Yamikani Yehova, tamandani dzina lake; mulengeze ntchito zake pakati pa mitundu ya anthu, ndipo mulalike kuti dzina lake ndi lopambana.

Verse Image for Yesaya 12:4

Yesaya 12:4 - Tsiku limenelo mudzati:
“Yamikani Yehova, tamandani dzina lake;
mulengeze ntchito zake pakati pa mitundu ya anthu,
ndipo mulalike kuti dzina lake ndi lopambana.

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 12:4