YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 11:6

Yesaya 11:6 CCL

Mʼmbulu udzakhala pamodzi ndi mwana wankhosa, kambuku adzagona pansi pamodzi ndi mwana wambuzi, mwana wangʼombe ndi mwana wa mkango adzadyera limodzi ndipo mwana wamngʼono adzaziweta.

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 11:6