YouVersion Logo
Search Icon

Yesaya 11:4

Yesaya 11:4 CCL

koma amphawi adzawaweruza mwachilungamo, adzaweruza mwachilungamo mlandu wa anthu osauka a dziko lapansi. Iye adzakantha dziko lapansi ndi mawu ake; atalamula Iyeyu anthu oyipa adzaphedwa.

Free Reading Plans and Devotionals related to Yesaya 11:4