YouVersion Logo
Search Icon

Eksodo 31:17

Eksodo 31:17 CCL

Tsiku la Sabata lidzakhala chizindikiro chamuyaya pakati pa Ine ndi Aisraeli chosonyeza kuti Yehova analenga za kumwamba ndi dziko lapansi kwa masiku asanu ndi limodzi ndi kuti pa tsiku lachisanu ndi chiwiri analeka kugwira ntchito napumula.”

Free Reading Plans and Devotionals related to Eksodo 31:17