YouVersion Logo
Search Icon

Mlaliki 2:26

Mlaliki 2:26 CCL

Munthu amene amakondweretsa Mulungu, Mulunguyo amamusandutsa wanzeru, wozindikira ndi wachisangalalo, koma wochimwa, Mulungu amamupatsa ntchito yosonkhanitsa ndi kusunga chuma kuti adzachipereke kwa amene Mulunguyo amakondwera naye. Izinso ndi zopandapake, nʼkungodzivuta chabe.

Free Reading Plans and Devotionals related to Mlaliki 2:26