YouVersion Logo
Search Icon

MACHITIDWE 16:27-28

MACHITIDWE 16:27-28 BLP-2018

Pamene anautsidwa kutulo mdindoyo, anaona kuti pa makomo a ndende panatseguka, ndipo anasolola lupanga lake, nati adziphe yekha, poyesa kuti am'ndende adathawa. Koma Paulo anafuula ndi mau aakulu, nati, Usadzipweteka wekha; tonse tili muno.