1
Alom 7:25
Nyanja
NTNYBL2025
Nimuyamika Mnungu uyo waniombola kupitila kwa Yesu kulisito! Chimwechi nde umo nili ine, kwa njelu zanga, nilitumikila thauko la Mnungu, nambho kwa thupi langa liniguza kuchata machimo.
Compare
Explore Alom 7:25
2
Alom 7:18
Nijhiwa kuti palibe chabwino chalichonjhe mkati mwanga, kuchokana ni umundhu wanga, pakuti nifuna kuchita chindhu chabwino nambho sinikhoza kuchita.
Explore Alom 7:18
3
Alom 7:19
Pakuti chijha chindhu chabwino nichifuna sinichichita, nambho choipa icho sinichifuna nde icho nichichita
Explore Alom 7:19
4
Alom 7:20
chipano ngati nichita icho sinichifuna, osati ine nichita nambho yajha machimo yakhala mkati mwanga nde yayo yachita.
Explore Alom 7:20
5
Alom 7:21-22
Chipano najhiwa chimwechi, kuti nifuna kuchita chindhu chabwino, nambho nijhipeza kuti chijha chilichoipa nde ichonisangha. Mumtima wanga, nilikondwela thauko la Mnungu.
Explore Alom 7:21-22
6
Alom 7:16
Ngati nichita chijha sinichifuna ine kuchita, pamenepo nivomela kuti lijha thauko ni la bwino.
Explore Alom 7:16
Home
Bible
Plans
Videos