Chipano wakwezedwe Mnungu uyo wakhoza kukuchitani anyiimwe mkhale nganganga mchikhulupililo ndande ya ujha Uthenga wa Bwino wa Yesu nidakulalikilani, kuchokana ni kuvunukuludwa visisi vidabisika kuyambila kale. Nambho chipano uzene uwu wavunukulidwa kwa njila ya malembo ya alosi, ni kwa lamulo la Mnungu wa muyaya wajhiwichidwa kwa maiko yonjhe, kuti wonjhe akhoze kukhulupilila Yesu Kilisito ni kuchita icho wachifuna.
Mnungu wali yokha ni uyo wali ni njelu zonjhe watamandidwe kupitila Yesu Kilisito, muyaya ni muyaya! Ikhale chimwecho.